Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 296 TIYENI Akhristu,

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

 

TIYENI Akhristu,
Nkhondo tigwire;
Yesu Mbuye wathu
Atitsogolera.
Mfumu yathu mwini
Atipatsa moyo;
Taonanitu mbendera
Yailoŵa nkhondo!

Tiyeni Akristu,
Nkhondo tiigwire;
Yesu Mbuye wathu
Atitsogolera

Nkhondo ya Satana
Idzakuthaŵani;
Tiyeni Akristu,
Kaipambaneni.
Idzanjenjemera
Mukapfu’litsatu;
Imbitsanitu anzathu,
Mau mukwezetse.

Mpingo wa Mulungu
Uli ngati nkhondo;
Titsagane nawo
Ana a Mulungu.
Sitipatukana,
Ndifetu amodzi;
Ch’yembekezo, chikondano,
Chonse ndi chimodzi.

Zonse zapadziko
Zidzamalizira,
Koma mpingo wake
Uli chikhalire;
Udzakhala ndithu
Mphamvu za Satana,
Yesu analonjezetsa,
Mawuwo sakana.

Tiyeni anzathu
Tizithandizana;
Imbirani nafe
Nyimbo zopambana
Kristu ayenera
Mphamvu ndi ulemu;
Komwe kuli Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
Next: Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version