Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 294 POYESEDWA ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 294 POYESEDWA ine

Hymn 294 POYESEDWA ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 294 POYESEDWA ine

 

POYESEDWA ine
Yesu mudzetu,
Mundipempherere
Ndisachimwetu.
Mukaona kuti
Ndilefukatu,
Mbuye mndilimbitse
Nazo mphamvutu.

Ndi zapansi pano
Ndikokedwadi,
Koma ndi chisoni
Mndiphunzitsedi;
Ndisaiŵalire
Za Getsemane,
Pena mtanda wanu
Yesu Mbuye ’Nu.

Mukandipweteka,
Ndipirirapo:
Nsembe yanga ndiyo,
Landirani ’yo.
Ndikachita mantha Sindithaŵa ’yi:
Mtima udzalimba,
Ndidzaima nji!

Pakumalizidwa
Moyo wangawu,
Pomwalira ine,
Mudze Mbuyetu.
Ndidzadzipereka
M’manja mwanumo:
Mpulumutsi Yesu
Mndilandireko.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version