Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 294 POYESEDWA ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 294 POYESEDWA ine

Hymn 294 POYESEDWA ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 294 POYESEDWA ine

 

POYESEDWA ine
Yesu mudzetu,
Mundipempherere
Ndisachimwetu.
Mukaona kuti
Ndilefukatu,
Mbuye mndilimbitse
Nazo mphamvutu.

Ndi zapansi pano
Ndikokedwadi,
Koma ndi chisoni
Mndiphunzitsedi;
Ndisaiŵalire
Za Getsemane,
Pena mtanda wanu
Yesu Mbuye ’Nu.

Mukandipweteka,
Ndipirirapo:
Nsembe yanga ndiyo,
Landirani ’yo.
Ndikachita mantha Sindithaŵa ’yi:
Mtima udzalimba,
Ndidzaima nji!

Pakumalizidwa
Moyo wangawu,
Pomwalira ine,
Mudze Mbuyetu.
Ndidzadzipereka
M’manja mwanumo:
Mpulumutsi Yesu
Mndilandireko.

Post navigation

Previous: Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
Next: Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version