Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

 

M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
Ndiyenderane nanu;
E, nditsamire pa ‘nu Yesu,
Panjira yonseyi.

Ndiwonetsere kuunika,
Kokoma kwanu Yesu!
Yabwino mbiri ndibukitse,
Yokondweretsayo.

Chitsime chakuyera ine,
Ndifananetu nacho;
Mundigwiritse ntchito zanu,
E, zanu zokhazo.

Mulamulire mtima, Yesu,
Ndi chifuniro changa;
Mulowe mwanga ngati Mfumu;
Kuti ndimvere ‘Nu.

Ndimamva njala kuno, Yesu,
Yakufunitsa Inu;
Kumwamba kwanu ndikukhumba.
Kukondwa nanuko.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version