Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

  1. Home   »  
  2. Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

 

MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
(Yesu) Yemwe anafera ine,
Ndiye anandiwombola;
Yesu, Yesu.

Mwazi wake ndi chitsime changa,
(Yesu) Pamene ndikasambamo
Zochimwa zanga zidzatha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
(Yesu) ngati mundisiya ndekha,
Kukhala ndekha sinditha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndisekere
(Yesu) Inu Mpulumutsi wanga
Pamene mukhala nane;
Yesu, Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version