Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

  1. Home   »  
  2. Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

 

NGATI mtima sumakonda
Yesu supumula bwino;
Mbuye, suwu mtima wanga,
Ndiwo wanu, mulandire.

Dziko lonse ndilitaya;
Ndikondetsa Yesu Mbuye;
An’komera kopambana
Andikondweretsa ndiye.

Ndakudani, mnandikonda
Ndi kukhetsa mwazi wanu.
Simuleka kundikonda;
Ine sindidzalekanso.

Mndisungire mtima wanga,
Uzikhulupira Inu,
Kuti moyo wanga wonse
Ubisaletu mwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version