Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

  1. Home   »  
  2. Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

 

NGATI mtima sumakonda
Yesu supumula bwino;
Mbuye, suwu mtima wanga,
Ndiwo wanu, mulandire.

Dziko lonse ndilitaya;
Ndikondetsa Yesu Mbuye;
An’komera kopambana
Andikondweretsa ndiye.

Ndakudani, mnandikonda
Ndi kukhetsa mwazi wanu.
Simuleka kundikonda;
Ine sindidzalekanso.

Mndisungire mtima wanga,
Uzikhulupira Inu,
Kuti moyo wanga wonse
Ubisaletu mwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
Next: Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version