Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

 

KHALA chete mtima wanga
Mlungu wako ndiye Mfumu;
Zinthu zonse zisinthika,
Mlungu ndi wachikhalire.

(Khala chete, Chidzakupinga n’chiyani?
Usaope, Mulungu ali nawe.)

Anthu onse pansi pano
Sakhutitsa mtima wawo;
Amadera zinthu zawo,
Namakhumba zakutali.

Khala chete mtima wanga,
Zikwanire zinthu zako;
Usakhumbe zapansipa
Koma Mlungu wako yekha.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 491 N’takafika kwanu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version