Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

Chichewa Christian Hymns

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

 

KHALA chete mtima wanga
Mlungu wako ndiye Mfumu;
Zinthu zonse zisinthika,
Mlungu ndi wachikhalire.

(Khala chete, Chidzakupinga n’chiyani?
Usaope, Mulungu ali nawe.)

Anthu onse pansi pano
Sakhutitsa mtima wawo;
Amadera zinthu zawo,
Namakhumba zakutali.

Khala chete mtima wanga,
Zikwanire zinthu zako;
Usakhumbe zapansipa
Koma Mlungu wako yekha.

Exit mobile version