Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

 

MBUYANGA Yesu,
mundigwire dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
Next: Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 294 Yesu anali khanda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version