Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

 

MBUYANGA Yesu,
mundigwire dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version