Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

 

TITAME Mlungu Wakumwamba,
Timwimbire nyimbo,
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo.

(Timwimbire nyimbo,
Timwimbire nyimbo!
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo)

Poyamba paja analenga
Zonse dziko muno,
Tsopano lomwe azisunga
Zonse zili moyo.

Tinasokera ngati nkhosa,
Moyo tinataya,
Tinakondwera ndi zoipa
Zonse tinatsata.

Komweko titasaukira,
Titafuna kufa,
Atate anatilondola
Naitana ife.

Tiyeni tizipita kwathu,
Tisasokerenso,
Tilape m’mtima kuti
tikakhale ndi Mulungu.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version