Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 239 TILI ndi mtendere

  1. Home   »  
  2. Hymn 239 TILI ndi mtendere

Hymn 239 TILI ndi mtendere

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 239 TILI ndi mtendere

 

TILI ndi mtendere
Wopambanatu,
Monga ngati mtsinje
Mumitimamo;
Koma mtsinje uno
Umayenda phee,
Nthaŵi zonse mtima
Nutonthozabe.

Tikakhulupira
Mlungu wathuyo,
Tidzaona mwayi
Ndi mtenderewo.

Dzanja la Mulungu
Litisunga nji!
Nkhondo ya Satana
Sitiopa ’yi.
Zaphokoso zonse
Ndi zoopsyazo
Sizibvuta mtima,
Siziloŵamo.

Masauko athu
Ndi zokondwazo,
Azilola zonse
Ndi Atatewo.
Pokhulupirira
Tidzapezabe
Kuti mtima wake
Utikonda ’fe.

YESU ndiye Mbuye wanga,
Ndamva Mawu akewo
Andilandira ine,
Nandipulumutsatu.
Mwalembedwa mukalata
Mawu ake omwewo,
Kuti iwo akumvera
Akalandiridwatu.

Ndinakahala wakuipa, Ndinamkana kalelo;
Koma Yesu waiŵala
Mphulupulu zangazo.

Wapumitsa mtima wanga,
Kaamba ndaphunziratu
Mau ake olembedwa
Mukalata mwakemo.

Mumvetu abwenzi athu,
Musakanirire ’yi;
Yesu aitana inu,
Zalembedwa zomwezi.

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version