Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 239 TILI ndi mtendere

  1. Home   »  
  2. Hymn 239 TILI ndi mtendere

Hymn 239 TILI ndi mtendere

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 239 TILI ndi mtendere

 

TILI ndi mtendere
Wopambanatu,
Monga ngati mtsinje
Mumitimamo;
Koma mtsinje uno
Umayenda phee,
Nthaŵi zonse mtima
Nutonthozabe.

Tikakhulupira
Mlungu wathuyo,
Tidzaona mwayi
Ndi mtenderewo.

Dzanja la Mulungu
Litisunga nji!
Nkhondo ya Satana
Sitiopa ’yi.
Zaphokoso zonse
Ndi zoopsyazo
Sizibvuta mtima,
Siziloŵamo.

Masauko athu
Ndi zokondwazo,
Azilola zonse
Ndi Atatewo.
Pokhulupirira
Tidzapezabe
Kuti mtima wake
Utikonda ’fe.

YESU ndiye Mbuye wanga,
Ndamva Mawu akewo
Andilandira ine,
Nandipulumutsatu.
Mwalembedwa mukalata
Mawu ake omwewo,
Kuti iwo akumvera
Akalandiridwatu.

Ndinakahala wakuipa, Ndinamkana kalelo;
Koma Yesu waiŵala
Mphulupulu zangazo.

Wapumitsa mtima wanga,
Kaamba ndaphunziratu
Mau ake olembedwa
Mukalata mwakemo.

Mumvetu abwenzi athu,
Musakanirire ’yi;
Yesu aitana inu,
Zalembedwa zomwezi.

Post navigation

Previous: Hymn 238 MULUNGU wanga,
Next: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version