Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

 

TATE ndili mwana wanu,
Nkana ndinachimwa,
Ndingolirira kwa Inu;
Khululukireni.

Machimo anga ngambiri
Osaŵerengeka,
Ndingoyang’ana kwa Inu;
Khululukireni.

Ndinachimwa poganiza
Ndi polankhulanso,
M’ntchito zanga ndachimwanso;
Khululukireni.

Ndinachita mphulupulu,
Ndinakunyozani,
M’ntchito zanga ndalephera;
Khululukireni.

Zonse ndinakonda kale
Ndi zopanda pake,
Sindinakhuta nazotu;
Khululukireni.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version