Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

 

TATE ndili mwana wanu,
Nkana ndinachimwa,
Ndingolirira kwa Inu;
Khululukireni.

Machimo anga ngambiri
Osaŵerengeka,
Ndingoyang’ana kwa Inu;
Khululukireni.

Ndinachimwa poganiza
Ndi polankhulanso,
M’ntchito zanga ndachimwanso;
Khululukireni.

Ndinachita mphulupulu,
Ndinakunyozani,
M’ntchito zanga ndalephera;
Khululukireni.

Zonse ndinakonda kale
Ndi zopanda pake,
Sindinakhuta nazotu;
Khululukireni.

Post navigation

Previous: Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
Next: Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version