Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

 

AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
Nanga inu? Nanga inu?
Tapeza chipulumutso ndithu;
Nanga inu?

Masiku onse timakondwera
Pakumva Mawu ake a Yesu;
Wolalikira tidzamumvera;
Nanga inu?

Ife tiyembekezera YESU,
Nanga inu? Nanga inu?
Chimwemwecho chilimumtimamu;
Nanga inu?

Titasokera tinabwerera,
Nanga inu? Nanga inu?
Tidziŵa kuti ndiwo uchimo;
Nanga inu?

Tinachoka munjira ya imfa,
Nanga inu? Nanga inu?
Takopeka ndi Mawu a Yesu;
Nanga inu?

Post navigation

Previous: Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
Next: Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version