Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

  1. Home   »  
  2. Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

 

ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Ŵalira Yesu m’ntchito zakozi,
Ŵalira Yesu pofanana ndi
Ambuyathu Yesu Kristu.

Tiŵaliretu, tiŵaliretu
Ambuye Yesu wotikonda ’fe;
Mlemekeze ’Ye tsiku lonseli,
Ine tiŵalire Yesu.

Ŵalira Yesu pazobvutazo,
Ŵalira Yesu pakukondwanso,
Ŵalira Yesu, imbirani ’nu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Ŵalira Yesu wolimbitsayo,
Ŵalira Yesu m’moyo monsemo
Ŵalira Yesu; tidzaonatu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version