Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

  1. Home   »  
  2. Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

 

MTIMA wanga uyamike,
Mfumu ya Kumwambako,
Anandiwombola ine;
Nanditsuka m’mtimamo.

Ife tonse, ife tonse,
Tiyamike Mlunguyo.

Tiyamike Mulungu wathu,
Kaamba ka chifundocho;
Nthaŵi zonse sasinthika,
Mlungu wathu yemweyo.

Nthaŵi zonse monga Tate,
Atisamaliratu;
Atisunga m’manja mwake,
Atipulumutsatu.

Anthu a mitundu yonse,
Ndiponso a Kumwamba;
Yamikani Mungu wathu,
Ndiye wakukomatu.

Anthu onse, anthu onse,
Yamikani Mlunguyo.

Post navigation

Previous: Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
Next: Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hello world!
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version