Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

 

USANABADWE, Yeremiya,
Ine ndinakudziwa;
Ndipo ndinakupatula,
Kuti ukhale mneneri.

Ulalike mawu anga Yeremiya,
Pita ukalalikire
Mawu anga;
Mawu anga Yeremiya.

“Usaopetu nkhope zawo,
Ine ndili ndi iwe;
Kuti ndikulanditsetu,
Iweyo,” ati Yehova.

Usaganize ndiwe mwana,
Iwe udzanka konse;
Kumene ndidzakutuma,
Kuti ukalalikire.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version