Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

 

USANABADWE, Yeremiya,
Ine ndinakudziwa;
Ndipo ndinakupatula,
Kuti ukhale mneneri.

Ulalike mawu anga Yeremiya,
Pita ukalalikire
Mawu anga;
Mawu anga Yeremiya.

“Usaopetu nkhope zawo,
Ine ndili ndi iwe;
Kuti ndikulanditsetu,
Iweyo,” ati Yehova.

Usaganize ndiwe mwana,
Iwe udzanka konse;
Kumene ndidzakutuma,
Kuti ukalalikire.

Post navigation

Previous: Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
Next: Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version