Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

 

POLUMIDWA ndi njokazo,
M’chipululumo;
Aisrayeli ‘nafa,
Ambiri.

Mwachikondi Mlungu “Tate,
Nawuza Mose:
“Yamkuwa njoka upange,
Msangatu.”

Amene akayang’ane,
Njoka pamtengo;
Ngakhaletu walumidwa,
Achira.

Satana amatiluma,
Ndi uchimowo;
Mwana Mlungu natifera,
Pamtanda.

Tiyang’ane pamtandapo,
Tipulumuke;
Adzatitenga kupita,
Kwawoko.

Post navigation

Previous: Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
Next: Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version