Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

  1. Home   »  
  2. Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

 

MULI ndi ludzu, idzani
Kumadzi amoyo
Imwani monse kolere
Kuchitsime konko.

Munka kangati kulaŵa
Madzi onyengera?
Musataye mphamvu yanu,
Musataye chuma.

Imvani, Yesu akuti;
“Chuma ndili nacho,
Landirani, yemwe amva
Akhale ndi moyo.”

Funani Mlungu tsopano.
Akulindirani;
Iye ndiye wachifundo,
Akulandirani.

Ali wokhululukira;
Imvani ananu:
Mtima wake usiyana
Ndi mitima yathu.

Monga m’Mwamba mupambana
Zonse pansi pano;
Choncho maganizo ake
Apitira athu.

Anthu onse a padziko
Adzamvera Mlungu:
Adzakhala ndi chimwemwe,
Nadzamtama ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version