Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

 

NDITAMATU Ambuyangayu,
Moyo wanga wonse ndidzam’tamatu;
Ndiponso m’dziko lakumwambako.
Masiku anga onse ndidzam’lemekeza Iye,
Sindizaleka konsekonse mmene ndili moyotu;
Pa dziko pano pena m’Mwambamo.

Ndiye wokondwa, E, munthuyo,
Wokhulupirira Mlungu yekhadi;
Wolenga dziko, nyanja, zonsezi.
Choona chake chonse chingokhalatu chosatha,
Apulumutsa onse namadyetsa anthu akewo;
Wokonda ndiye Mlungu wathuyo.

Mlungu kuwona athiratu,
Inde m’maso awo osapenyawo;
Natuma akumvera mpumulo.
Amathandiza inde aulendo awo ofokatu,
Akazi amasiye, maka ndi ana’wo onsewo;
Olira otonthoza mtimadi.

Nditama Ambuyangayu,
Moyo wanga wonse ndidzam’tamatu;
Ndiponso m’dziko la Kumwambako.
Masiku anga onse ndidzam’lemekeza Iye,
Sindidzaleka konsekonse mmene ndili moyotu;
Padziko pano pena m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
Next: Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version