Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

 

NDITAMATU Ambuyangayu,
Moyo wanga wonse ndidzam’tamatu;
Ndiponso m’dziko lakumwambako.
Masiku anga onse ndidzam’lemekeza Iye,
Sindizaleka konsekonse mmene ndili moyotu;
Pa dziko pano pena m’Mwambamo.

Ndiye wokondwa, E, munthuyo,
Wokhulupirira Mlungu yekhadi;
Wolenga dziko, nyanja, zonsezi.
Choona chake chonse chingokhalatu chosatha,
Apulumutsa onse namadyetsa anthu akewo;
Wokonda ndiye Mlungu wathuyo.

Mlungu kuwona athiratu,
Inde m’maso awo osapenyawo;
Natuma akumvera mpumulo.
Amathandiza inde aulendo awo ofokatu,
Akazi amasiye, maka ndi ana’wo onsewo;
Olira otonthoza mtimadi.

Nditama Ambuyangayu,
Moyo wanga wonse ndidzam’tamatu;
Ndiponso m’dziko la Kumwambako.
Masiku anga onse ndidzam’lemekeza Iye,
Sindidzaleka konsekonse mmene ndili moyotu;
Padziko pano pena m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version