Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

 

MZIMU Woyera, mudzetu,
Tiyeretsedwe m’mtimamu;
Mupatse anthu anuwa
Mitulo yanu yonseyo.

Kudzoza kwa Kumwambako
Kutitonthoza m’mtimamo,
Ndi kutidzutsa m’moyomu,
Tikhale okondanatu.

Pankhope pathu mthirepo
Chisomo chanu chijacho;
Mtendere mutininkhebe,
Mutiyendetse ponse phee!

Tionetseni tonsetu
Umodzi wanu wonsemo,
Atate, Mwana, Mzimu ’Nu
Tiimbe Nthaŵi zonsezo:

Titamire Nthaŵi zonse
’Tate, Mwana, Mzimu, Nonse.
Amen

Post navigation

Previous: Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
Next: Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hello world!
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version