Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

 

MZIMU Woyera, mudzetu,
Tiyeretsedwe m’mtimamu;
Mupatse anthu anuwa
Mitulo yanu yonseyo.

Kudzoza kwa Kumwambako
Kutitonthoza m’mtimamo,
Ndi kutidzutsa m’moyomu,
Tikhale okondanatu.

Pankhope pathu mthirepo
Chisomo chanu chijacho;
Mtendere mutininkhebe,
Mutiyendetse ponse phee!

Tionetseni tonsetu
Umodzi wanu wonsemo,
Atate, Mwana, Mzimu ’Nu
Tiimbe Nthaŵi zonsezo:

Titamire Nthaŵi zonse
’Tate, Mwana, Mzimu, Nonse.
Amen

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version