Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

 

MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Ndi kundidzaza moyo wanuwo,
Kuti ndikonde zomwe mukondanso,
Ndichite chomwe mumachitanso.

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Mpaka mtimanga ukayeretu,
Ndipo zokhumba zanga zilingane
Nazo zanuzo zakuyera mbuu!

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Mpaka ndikhale wanu nokhatu;
Ayeretsedwe makhalidwe anga
Ndi mphamvu yanu yondisunga nji!

Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Kuti inedi ndisafe ’yitu,
Koma ndikhale nanu m’moyo womwe
Wangwiro ndi wa nthaŵi zonsetu.

Post navigation

Previous: Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
Next: Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 94 KHAMULO liliko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version