Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

 

MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
E, ngati mvula m’dziko lakuuma,
Ndikhale munda wanu wakupatsa
Zipatso zoyenera Mbuyeyo.

Mphunzitsi, ndinu mudziŵitse ine
Chikondi chanu chija chachikulu;
Lembani mawu anu pamtimanga,
Kuti ndikhumbukire zanuzo.

Wosangalatsa, ine ndikalira
Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe;
Mundigoneke pachifuwa chake
Cha Yesu kuti ndikakondwepo.

Wotsogolera, munditsogolere
Kuti n’kafike kwawo kwa Atate,
Nditsate Yesu ndikuyendayenda
M’njira yomweyo anapondamo.

Mthandizi ndinu, mndithangate ine
Kupempha bwino izo zindisoŵa.
Kupempha monga Mlungu amafuna
Kulingalira zake zokhazo.

Mzimu Woyera, n’dzipereke ndense,
Mundichitire ntchito yaikulu;
Mtima woyera ndi womvera mpatse,
Wodzala ndi chikondi chanucho.

Post navigation

Previous: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
Next: Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version