Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

 

MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
E, ngati mvula m’dziko lakuuma,
Ndikhale munda wanu wakupatsa
Zipatso zoyenera Mbuyeyo.

Mphunzitsi, ndinu mudziŵitse ine
Chikondi chanu chija chachikulu;
Lembani mawu anu pamtimanga,
Kuti ndikhumbukire zanuzo.

Wosangalatsa, ine ndikalira
Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe;
Mundigoneke pachifuwa chake
Cha Yesu kuti ndikakondwepo.

Wotsogolera, munditsogolere
Kuti n’kafike kwawo kwa Atate,
Nditsate Yesu ndikuyendayenda
M’njira yomweyo anapondamo.

Mthandizi ndinu, mndithangate ine
Kupempha bwino izo zindisoŵa.
Kupempha monga Mlungu amafuna
Kulingalira zake zokhazo.

Mzimu Woyera, n’dzipereke ndense,
Mundichitire ntchito yaikulu;
Mtima woyera ndi womvera mpatse,
Wodzala ndi chikondi chanucho.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version