Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,

Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,

 

CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
Tim’lambire Mbuye;
Tikweze nyimbo yakukondwa kuli ‘Ye,
Tim’gwadiretu.

Dzinja lokondweretsa lafikanso, litapumatu,
Tim’lambire Mbuye;
Mvula igundanso,
Mulungu wotikonda ‘fe,
Tim’gwadiretu.

Dziko lonse lili kukondwa, mlengalenga, mpheponso,
Tim’lambire Mbuye;
Zapansi pano zonse zim’tamandire,
Mulungu wathuyo,
Tim’gwadiretu.

Maluwa abwino aphuka m’mapiri, ndi m’madambomo,
Tim’lambire Mbuye;
Masamba ‘awisi, aang’ono agwedezekanso,
Tim’gwadiretu.

Zanu zapansi n’zokoma
Mbuye; tikondwera ‘fe,
Tim’lambire Mbuye;
Koma kwanu Kumwamba komwe kwapambanatu,
Tim’gwadiretu.

Nafenso tidzauka kwa
‘kufa ngati maluwawo,
Tim’lambire Mbuye;
Oyera mtima adzavala mbuu! pakudza Khrisituyo,
Tim’gwadiretu.

Tidzakhala naye nthawi zonse, ndi kuyimbako,
Tim’lambire Mbuye;
Kumene moyo wa anthu okhululukidwa uli wokomatu,
Tim’gwadiretu.
Aleluya, Amen!

Post navigation

Previous: Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
Next: Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version