Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

 

TIYAMIKE Ambuye,
Chifukwa chotilola,
Kulowa m’chaka chino m’tisunge;
Sitingathe ‘fe tokha,
Kuyenda m’chaka chonse;
Ambuye m’titsogoze,
M’tisunge.

M’tisunge, m’tisunge,
Yesu tikupemphani m’tisunge;
Ife timalephera kuyenda m’njira tokha;
Yesu tikupemphani m’tisunge.

Dziko lapansi pano timangoyenda chabe,
Wosaganiziranso za moyo;
Timaganiza kuti moyowu sudzathanso,
Ambuye m’tikumbutse leroli.

Moyowu ngwapafupi, monga kugwa kwa tsamba,
Monga kumanga mtolo m’tisunge;
Ambuye m’tidalitse,
Nthawi isanafike;
Kuti tingataike m’tisunge.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version