Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

 

TIYAMIKE Ambuye,
Chifukwa chotilola,
Kulowa m’chaka chino m’tisunge;
Sitingathe ‘fe tokha,
Kuyenda m’chaka chonse;
Ambuye m’titsogoze,
M’tisunge.

M’tisunge, m’tisunge,
Yesu tikupemphani m’tisunge;
Ife timalephera kuyenda m’njira tokha;
Yesu tikupemphani m’tisunge.

Dziko lapansi pano timangoyenda chabe,
Wosaganiziranso za moyo;
Timaganiza kuti moyowu sudzathanso,
Ambuye m’tikumbutse leroli.

Moyowu ngwapafupi, monga kugwa kwa tsamba,
Monga kumanga mtolo m’tisunge;
Ambuye m’tidalitse,
Nthawi isanafike;
Kuti tingataike m’tisunge.

Post navigation

Previous: Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
Next: Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version