Chichewa Christian Hymns
Hymn 412 MOYO uli pafupi,
MOYO uli pafupi,
Monga kugwa kwa tsamba,
Ndikumanga mitolo kangaza;
Usachedwe m’zoipa,
Sudzapeza mpumulo;
Ndipo sadzakuyankha,
Kangaza.
Kangaza, kangazatu,
Yesu ali kuyitana, kangaza;
Usachedwe m’zoipa,
Sudzapeza mpumulo;
Ndipo sadzakuyankha,
Kangaza.
Unyamata ngovuta,
Umabwera nupita,
Ndipo sadzakuyankha kangaza;
Usachedwe m’zoipa,
Sudzapeza mpumulo;
Ndipo sadzakuyankha
Kangaza.