Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 405 POLENGA dzikoli

  1. Home   »  
  2. Hymn 405 POLENGA dzikoli

Hymn 405 POLENGA dzikoli

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 405 POLENGA dzikoli

 

POLENGA dzikoli
Pakumva Inudi,
Kwayeratu;
Mumve pempheroli,
Ndipo pamenepo
Palibe mawuwo,
Muŵaletu.

Inu wakudzatu
Kuŵachiritsadi
Anthendawo,
Kupatsa moyowo,
Kuona m’masomo,
Pa anthu onsewo
Muŵaletu.

Mzimu woonadi
Ndi wachikondicho,
Idzanitu;
Muunikirepo
Pali zamdimazo,
Pa dziko ponsepo
Muŵaletu.

Inu atatuwo,
Wodala Mlunguyo,
Timveretu;
Pa dziko ponsepo
Muchotse mdimawo,
Mutume Mawuwo,
Muŵaletu.

Post navigation

Previous: Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
Next: Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version