Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 405 POLENGA dzikoli

  1. Home   »  
  2. Hymn 405 POLENGA dzikoli

Hymn 405 POLENGA dzikoli

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 405 POLENGA dzikoli

 

POLENGA dzikoli
Pakumva Inudi,
Kwayeratu;
Mumve pempheroli,
Ndipo pamenepo
Palibe mawuwo,
Muŵaletu.

Inu wakudzatu
Kuŵachiritsadi
Anthendawo,
Kupatsa moyowo,
Kuona m’masomo,
Pa anthu onsewo
Muŵaletu.

Mzimu woonadi
Ndi wachikondicho,
Idzanitu;
Muunikirepo
Pali zamdimazo,
Pa dziko ponsepo
Muŵaletu.

Inu atatuwo,
Wodala Mlunguyo,
Timveretu;
Pa dziko ponsepo
Muchotse mdimawo,
Mutume Mawuwo,
Muŵaletu.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version