Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

  1. Home   »  
  2. Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

 

MONGA zomera zonsezo
Zikula ponsepo,
Mulungu mumeretsazo,
Momwemo anawo.

Munali mwana, Yesu ’Nu
Wamng’ono kalelo,
Ndi munakula m’msinkhu ndi
Kutama ’Tatewo.

Ndi ife tinga, mbewuzo
Zomera m’mundawo;
Mumtima mutidyetsedi,
Tikule bwinomo;

Ndi kutsukidwa m’mwazimo
Mumtima mwathu mbee,
Tionetsedwe konseko
A Mlungu ana ’ke.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version