Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 356 YESU Mbuye onani,

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

 

YESU Mbuye onani,
Tadza poyitana Inu;
M’dzina lanu tifika,
Osekera kwa Atate.
M’khale nafe Inu nokha,
Tikayimba n’kupemphera.

Mbuye, Mzimu Woyera,
Munapatsa ana anu;
Kukalonga mumtima,
Mawu ndipo mvano womwe.
Zinthu zonse pansi pano,
Sizikondweretsa ife.

Mzimu, m’longe m’mtimamo,
Maphunziro achifundo;
Timve lero ndi mawa,
Ndi masiku onse: Yesu!
Ndipo M’mwamba tidzawona,
Tidazimva pansi pano.

Post navigation

Previous: Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
Next: Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 589 Koma ineyu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version