Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

 

KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Ndadzikundikira chuma Kumwambako;
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye, ndi ‘Nu Bwenzi langa ndithu.
Ndichitenji ngati Kumwamba sikwathu?
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
Mpulumutsi wanga wandikhu’lukira;
Adzandipyoletsa pamene ndafoka,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye watsogola ku Ulemerero,
Ndifuna kugwira dzanja lake konko;
Andidikiranso pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mu Ulemelero tidzakhala m’yaya,
Oyera mtimawo ali kulambira;
Ati: “Aleluya kwa Mlungu wamphamvu,”
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version