Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

  1. Home   »  
  2. Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

 

NGATI mtima sumakonda
Yesu supumula bwino;
Mbuye, suwu mtima wanga,
Ndiwo wanu, mulandire.

Dziko lonse ndilitaya;
Ndikondetsa Yesu Mbuye;
An’komera kopambana
Andikondweretsa ndiye.

Ndakudani, mnandikonda
Ndi kukhetsa mwazi wanu.
Simuleka kundikonda;
Ine sindidzalekanso.

Mndisungire mtima wanga,
Uzikhulupira Inu,
Kuti moyo wanga wonse
Ubisaletu mwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version