Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

  1. Home   »  
  2. Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

 

NGATI mtima sumakonda
Yesu supumula bwino;
Mbuye, suwu mtima wanga,
Ndiwo wanu, mulandire.

Dziko lonse ndilitaya;
Ndikondetsa Yesu Mbuye;
An’komera kopambana
Andikondweretsa ndiye.

Ndakudani, mnandikonda
Ndi kukhetsa mwazi wanu.
Simuleka kundikonda;
Ine sindidzalekanso.

Mndisungire mtima wanga,
Uzikhulupira Inu,
Kuti moyo wanga wonse
Ubisaletu mwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
Next: Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 260 Angelo aitana,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version