Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga

 

NDILIKUMVA m’mtima mwanga
Mau ake a MbuyAnga,
Ati, “Ndakukonda iwe,
Kodi undikonda Ine?”

Ati; “Mwana, kumbukira
Zonse ndinakuchitira;
Ndakukonda, ndakufera,
Ndakufuna posokera.

“Ku zoipa zonse zako,
Goli la pakhosi pako,
Ndi kunthenda zosautsa
Ndine ndakupulumutsa

“Kodi mayi wobereka
Mwana wake adzamleka
Pena adzamwiŵalira,
Koma ndikukumbukira.

“Nthaŵi ilikudza yonse
Sindisinthanika konse;
Imfa sindiletsa Ine
Ndisakondekonde iwe.

“Ine ndidzakuonetsa
Zonse zakukondweretsa
Za Kumwamba zanga izo,
Mwana, sundikonda ine?”

Ambuyanga, ndalephera,
Mwachisoni ndipemphera
Mundipatse ine ndithu
Mtima wakukonda Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version