Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

  1. Home   »  
  2. Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

 

NDI MISOZI, ndi chisoni,
Ndiliratu kwa Inu Yesu;
Ndi chifundo chandigwira,
Ndilira kutí ndili wanu

E! Kwa Inu, E! Kwa Inu!
Ndilira kuti ndili wanu.

Mbuye Yesu ndi Atate,
Mundiwona ndili wosowa;
Ndimasowa Mzimu wanu,
Kuinga zonse za mumtima.

Mtenderewo, wosanyenga,
Ndilira ine m’mtima mwanga;
Kundimvetsa chimwemwetu,
Ndilira ine m’mtima mwanga.

Kalekale ndinathawa,
Ndinakana kumvera Inu;
Koma lero ndamva kuti,
Muli mwini wake wa moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version