Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

  1. Home   »  
  2. Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

 

NDI MISOZI, ndi chisoni,
Ndiliratu kwa Inu Yesu;
Ndi chifundo chandigwira,
Ndilira kutí ndili wanu

E! Kwa Inu, E! Kwa Inu!
Ndilira kuti ndili wanu.

Mbuye Yesu ndi Atate,
Mundiwona ndili wosowa;
Ndimasowa Mzimu wanu,
Kuinga zonse za mumtima.

Mtenderewo, wosanyenga,
Ndilira ine m’mtima mwanga;
Kundimvetsa chimwemwetu,
Ndilira ine m’mtima mwanga.

Kalekale ndinathawa,
Ndinakana kumvera Inu;
Koma lero ndamva kuti,
Muli mwini wake wa moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
Next: Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version