Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

 

PENYETSETSA Yesu,
Mtima wosauka; Anafera iwe,
Idza, nupumule.
Iye anachotsa
Nsoni ndi zoipa;
Penyetsetsa Yesu,
Ndi kukhulupira.

Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa;
Yachuluka ntchito,
Mphamvu idzakula.
Akonzera kwawo
Nyumba zokhalamo;
Penyetsetsa Yesu,
Mtsatetu tsopano.

Penyetsetsa Yesu
Pogwirana nawo;
Nkhondo ikabvuta
Tamva Mbuye wako.
Achuluka’dani,
Iwe ungofoka;
Penyetsetsa Yesu,
Mantha adzachoka.

Ndipo pakuloŵa
M’dziko la Kumwamba,
Udzapeza komwe
Onse adzatama.
Mwa zoŵala zija
Za Kumwamba kwawo,
Udzapenya maso
Yesu Mbuye wako.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version