Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

 

PENYETSETSA Yesu,
Mtima wosauka; Anafera iwe,
Idza, nupumule.
Iye anachotsa
Nsoni ndi zoipa;
Penyetsetsa Yesu,
Ndi kukhulupira.

Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa;
Yachuluka ntchito,
Mphamvu idzakula.
Akonzera kwawo
Nyumba zokhalamo;
Penyetsetsa Yesu,
Mtsatetu tsopano.

Penyetsetsa Yesu
Pogwirana nawo;
Nkhondo ikabvuta
Tamva Mbuye wako.
Achuluka’dani,
Iwe ungofoka;
Penyetsetsa Yesu,
Mantha adzachoka.

Ndipo pakuloŵa
M’dziko la Kumwamba,
Udzapeza komwe
Onse adzatama.
Mwa zoŵala zija
Za Kumwamba kwawo,
Udzapenya maso
Yesu Mbuye wako.

Post navigation

Previous: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
Next: Hymn 163 MALO anachepa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version