Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

  1. Home   »  
  2. Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

 

MULI ndi ludzu, idzani
Kumadzi amoyo
Imwani monse kolere
Kuchitsime konko.

Munka kangati kulaŵa
Madzi onyengera?
Musataye mphamvu yanu,
Musataye chuma.

Imvani, Yesu akuti;
“Chuma ndili nacho,
Landirani, yemwe amva
Akhale ndi moyo.”

Funani Mlungu tsopano.
Akulindirani;
Iye ndiye wachifundo,
Akulandirani.

Ali wokhululukira;
Imvani ananu:
Mtima wake usiyana
Ndi mitima yathu.

Monga m’Mwamba mupambana
Zonse pansi pano;
Choncho maganizo ake
Apitira athu.

Anthu onse a padziko
Adzamvera Mlungu:
Adzakhala ndi chimwemwe,
Nadzamtama ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
Next: Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 891 Akakusowa malo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version