Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

  1. Home   »  
  2. Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

 

MULI ndi ludzu, idzani
Kumadzi amoyo
Imwani monse kolere
Kuchitsime konko.

Munka kangati kulaŵa
Madzi onyengera?
Musataye mphamvu yanu,
Musataye chuma.

Imvani, Yesu akuti;
“Chuma ndili nacho,
Landirani, yemwe amva
Akhale ndi moyo.”

Funani Mlungu tsopano.
Akulindirani;
Iye ndiye wachifundo,
Akulandirani.

Ali wokhululukira;
Imvani ananu:
Mtima wake usiyana
Ndi mitima yathu.

Monga m’Mwamba mupambana
Zonse pansi pano;
Choncho maganizo ake
Apitira athu.

Anthu onse a padziko
Adzamvera Mlungu:
Adzakhala ndi chimwemwe,
Nadzamtama ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version