Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

 

MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Kuyatsa moto m’mtima mwathu;
Ntchito ndi yanu kudzozera
Ndi kutininkha mphatsozo.

Kudzodza kwanu kutipatsa
Chimwemwe, moyo ndi mtendere;
Kuŵala kwanu kupenyetsa
A m’mdima ndi a m’ndendemo.

Mtima wodetsa mukonzere,
Chisomo chanu chakwanira;
Adani athu muthaŵitse

Mutidziŵitse ‘Tate wathu,
Ndi mwana wake ndinu Mmodzi.
Mnafuma kwa aŵiri onse,
Koma Mulungu Mmodziyo

Post navigation

Previous: Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version