Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,

 

MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Kuyatsa moto m’mtima mwathu;
Ntchito ndi yanu kudzozera
Ndi kutininkha mphatsozo.

Kudzodza kwanu kutipatsa
Chimwemwe, moyo ndi mtendere;
Kuŵala kwanu kupenyetsa
A m’mdima ndi a m’ndendemo.

Mtima wodetsa mukonzere,
Chisomo chanu chakwanira;
Adani athu muthaŵitse

Mutidziŵitse ‘Tate wathu,
Ndi mwana wake ndinu Mmodzi.
Mnafuma kwa aŵiri onse,
Koma Mulungu Mmodziyo

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version