Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

 

MBUYE Yesu adzabwera,
Asekere anthu onse;
Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
Adzabwera, adzabwera;
E! bwerani Mbuye wathu.

Dziko lino linaona
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
M’mene adzabwera Iye.
Adzabwera, adzabwera;
Timvomera, E! mubwere

Anthu anu amafoka,
Pa ulendo nasokera;
Ha! Adzaonana nanu
Atabvalanso zoyera.
Mudzabwera, mudzabwera;
Inde Mbuyetu mubwere.

Ndi chiyembekezo ichi
Sitikhala chete ife:
Tiimbitsa nyimbo zathu
Zakulemekeza Mlungu.
Adzabwera, adzabwera
E!! mubwere msanga YESU.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 171 M’manda munalibe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version