Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

 

MBUYE Yesu adzabwera,
Asekere anthu onse;
Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
Adzabwera, adzabwera;
E! bwerani Mbuye wathu.

Dziko lino linaona
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
M’mene adzabwera Iye.
Adzabwera, adzabwera;
Timvomera, E! mubwere

Anthu anu amafoka,
Pa ulendo nasokera;
Ha! Adzaonana nanu
Atabvalanso zoyera.
Mudzabwera, mudzabwera;
Inde Mbuyetu mubwere.

Ndi chiyembekezo ichi
Sitikhala chete ife:
Tiimbitsa nyimbo zathu
Zakulemekeza Mlungu.
Adzabwera, adzabwera
E!! mubwere msanga YESU.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version