Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

 

ALINKUDZA wansoni Munthu,
Wakukhala Kumwamba;
Alinkudza m’ulemerero,
Ndi Mwamuna wa mtanda.

Aleluya, Aleluya,
Alinkudza kwa ife;
Ndi chimwemwe
Tidzamkomana,
Pakufika Ambuye.

Alinkudza Ambuye Yesu,
Wakuphedwa pa dziko;
Alinkudza kukhala Mfumu,
Yoweruza mayiko.

Pakufika asonkhanitsa,
Anthu ake oyera;
Adzafuna mitundu yonse,
Omwe Iye ‘nafera.

Post navigation

Previous: Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
Next: Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 640 Anakwatira kale

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version