Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

 

ALINKUDZA wansoni Munthu,
Wakukhala Kumwamba;
Alinkudza m’ulemerero,
Ndi Mwamuna wa mtanda.

Aleluya, Aleluya,
Alinkudza kwa ife;
Ndi chimwemwe
Tidzamkomana,
Pakufika Ambuye.

Alinkudza Ambuye Yesu,
Wakuphedwa pa dziko;
Alinkudza kukhala Mfumu,
Yoweruza mayiko.

Pakufika asonkhanitsa,
Anthu ake oyera;
Adzafuna mitundu yonse,
Omwe Iye ‘nafera.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version