Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

  1. Home   »  
  2. Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

 

ONA Mwanawankhosayo
Wakuseza zakuipa zathu zonse.

Mwana wankhosa
Watisenzera
Zakuipa zathu zonse.

Anazenza m’thupi mwake;
Pakukhomedwa pa mtanda anali duu.

Ona pamtanda Yesuyo
Anabvutika chifukwa cha anthu’fe.

Imva kulira kwa Yesu
Pamene anasiyidwa muimfayo.

M’mwazi wake tisambamo;
Zichotsedwa zakuipa zathu zonse.

(Ona Mwana wa nkhosayo
Wakusenza zakuipa, zathu zonse.)

Post navigation

Previous: Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
Next: Hymn 50 PAUSIKU uja,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version