Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

 

KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Ndi Iye Mlungu Wamphamvu;
Angelo anapembedza
Mwana wakhanda Iyeyu.

Kamwana kaja ’nayamba
Kuonetsera Atate,
Lero anena Kumwamba:
“Tiana tidze kwa Ine.”

Tibwera ndi tianato
Kukabatiza ’menewa;
Muŵachitire chifundo.
M’ŵapatse Mzimu Woyera.

Angelo anu asunga
Tiana tathu tofoka;
Pa njira yanu tiyenda,
Mulembe m’Mwamba maina.

Mukonda nyimbo za ana,
Kokoma amaimbatu;
Ndi ana athu atama
Atate, Mwana ndi Mzimu.

Post navigation

Previous: Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version