Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

 

KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Ndi Iye Mlungu Wamphamvu;
Angelo anapembedza
Mwana wakhanda Iyeyu.

Kamwana kaja ’nayamba
Kuonetsera Atate,
Lero anena Kumwamba:
“Tiana tidze kwa Ine.”

Tibwera ndi tianato
Kukabatiza ’menewa;
Muŵachitire chifundo.
M’ŵapatse Mzimu Woyera.

Angelo anu asunga
Tiana tathu tofoka;
Pa njira yanu tiyenda,
Mulembe m’Mwamba maina.

Mukonda nyimbo za ana,
Kokoma amaimbatu;
Ndi ana athu atama
Atate, Mwana ndi Mzimu.

Post navigation

Previous: Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 1166 Masauko athu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version