Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

 

KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Ndi Iye Mlungu Wamphamvu;
Angelo anapembedza
Mwana wakhanda Iyeyu.

Kamwana kaja ’nayamba
Kuonetsera Atate,
Lero anena Kumwamba:
“Tiana tidze kwa Ine.”

Tibwera ndi tianato
Kukabatiza ’menewa;
Muŵachitire chifundo.
M’ŵapatse Mzimu Woyera.

Angelo anu asunga
Tiana tathu tofoka;
Pa njira yanu tiyenda,
Mulembe m’Mwamba maina.

Mukonda nyimbo za ana,
Kokoma amaimbatu;
Ndi ana athu atama
Atate, Mwana ndi Mzimu.

Post navigation

Previous: Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version