Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

 

PAPHIRI ndi padambo,
Ponsepo pali Mlungu;
Poyenda ife m’njira,
MpoYima pali Mlungu.
Kokwera Maganizo,
Komwe kuli Mlungu;
Kumwamba ndi pansipo,
Ponsepo pali Mlungu.

(Mulungu ali nane!)
(Ali nane, ali nane,
ali nane, ali nane, Aa!
Mulungu ali nane!)

Ndi maso Ambuyathu,
Apenyetsetsa ife;
Amadalitsa onse,
Okhulupi’ra Iye.
Amamva timbalame,
Naveka dziko lonse;
Sataya tizirombo,
Asunga zina zonse.

Okwaŵa pansi inu,
Oyenda m’madzi inu;
Oyesa dziko n’kwanu,
A m’mlengalenga inu.
Nonsenu ntchito zake,
Muwona tsiku n’tsiku;
Saleka kusamala,
Ndikudalitsa inu.

Nditama mphamvu yake,
Ya Mlungu yondizinga;
N’kafoka andilimbitsa,
N’kadwala andichiza.
Pakundisiya bwenzi,
Mulungu ali paja;
N’kaloŵa imfa ine,
Alipo Mlungu wanga.

Post navigation

Previous: Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
Next: Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version