Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

 

NDI Aleluya imbirani,
“Tate wathu wa Kumwamba,
Analenga zonse;
Chifundo chake chachikulu,
Nzeru, mphamvu ndi ufumu,
Tiyamike tonse.

Ndi Aleluya imbirani,
Yesu Khrisitu Mpulumutsi,
Anachoka kwawo;
Nakhala munthu pansi pano,
Nasawuka, natifera,
Natisiira mawu.

Ndi Aleluya imbirani,
Mzimu wake wakuyera,
Amakhala nafe:
Atilangiza za Mulungu,
Nayeretsanso mitima,
Ya Akhrisitu ife.

Mulungu wathu tiyamika,
“Tate, Mwana,
Mzimu yemwe,
Aleluya Inu;
Woyera Inu, ndi wamphamvu,
Muyenera anthu onse,
Agwadire Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hello world!
  • Hymn 514 Osanatu, osana,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version