Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

 

NDI Aleluya imbirani,
“Tate wathu wa Kumwamba,
Analenga zonse;
Chifundo chake chachikulu,
Nzeru, mphamvu ndi ufumu,
Tiyamike tonse.

Ndi Aleluya imbirani,
Yesu Khrisitu Mpulumutsi,
Anachoka kwawo;
Nakhala munthu pansi pano,
Nasawuka, natifera,
Natisiira mawu.

Ndi Aleluya imbirani,
Mzimu wake wakuyera,
Amakhala nafe:
Atilangiza za Mulungu,
Nayeretsanso mitima,
Ya Akhrisitu ife.

Mulungu wathu tiyamika,
“Tate, Mwana,
Mzimu yemwe,
Aleluya Inu;
Woyera Inu, ndi wamphamvu,
Muyenera anthu onse,
Agwadire Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Next: Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version