Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

 

ATATE wa Kumwambako,
Munawombola ife, ndi
Chikondi chanu chijacho;
Tiyamikira Inutu.

Ambuye Yesu Inutu,
Munabadwira anthu ’fe;
Munatifera tonse ’fe;
Tiyamikira Inutu.

Mzimu Woyera m’mtimamo
Tiyeretsedwe ndi Inutu;
Munatisunga bwinoli,
Tiyamikira Inutu.

Atate, Mwana, Mzimunso,
Ndinu Atatu, Mmodzitu
Ochimwa tikupemphani:
Mutikhululukire’fe

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version