Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

 

ATATE wa Kumwambako,
Munawombola ife, ndi
Chikondi chanu chijacho;
Tiyamikira Inutu.

Ambuye Yesu Inutu,
Munabadwira anthu ’fe;
Munatifera tonse ’fe;
Tiyamikira Inutu.

Mzimu Woyera m’mtimamo
Tiyeretsedwe ndi Inutu;
Munatisunga bwinoli,
Tiyamikira Inutu.

Atate, Mwana, Mzimunso,
Ndinu Atatu, Mmodzitu
Ochimwa tikupemphani:
Mutikhululukire’fe

Post navigation

Previous: Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
Next: Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version