Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

 

PAKWITANA Mbuye wanga
Potsiriza dzikoli,
Pakufika tsiku la kuŵalalo,
Posonkhana akumvera,
Pakuona Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Potuluka m’manda mwawo
Anthu ake onsewo,
Tidzasanganatu nawo nthaŵiyo.
Pakuluka osankhidwa,
Kunka naye Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Tisaleke kugwirabe
Ntchito ya Mulunguyo,
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli,
Ndi podzatha moyo wathu
Ndi zintchito zathuzo,
Tidzakondwerera naye komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version