Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

 

PAKWITANA Mbuye wanga
Potsiriza dzikoli,
Pakufika tsiku la kuŵalalo,
Posonkhana akumvera,
Pakuona Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Potuluka m’manda mwawo
Anthu ake onsewo,
Tidzasanganatu nawo nthaŵiyo.
Pakuluka osankhidwa,
Kunka naye Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Tisaleke kugwirabe
Ntchito ya Mulunguyo,
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli,
Ndi podzatha moyo wathu
Ndi zintchito zathuzo,
Tidzakondwerera naye komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
Next: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 74 IDZA wolema,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version