Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

 

MMENE Yesu adzabwera,
Adza ndi mitambo;
Ndipo diso lililonse,
Lidzamuwona Iye.

Adza, adza,
Adza ndi mitambo,
Ndipo diso lililonse;
Lidzamuwona Iye.

Adzakhala pa chimpando,
Choweruziracho;
Nadzayamba kuweruza,
Milandu ya anthu’fe.

Angelo ‘dzagwira ntchito,
Yolekanitsadi;
Anthu onse a padziko,
M’magulu awiritu.

Olugama nadzayima,
Kudzanja lamanja;
Koma onse oyipawo,
Mbali yakumanzere.

Akudzanja lamanjalo,
Kumoyo wosatha;
Akudzanja lamanzere,
Kumoto Wosathawo.

Post navigation

Previous: Hymn 76 E, MOYO wanga’we
Next: Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version