Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

 

A! MUTU wakuyera,
Wolaswa wachisoni,
Abveka Inu anthu
Ndi minga ya udani;
Ambuye mwafokatu
Ndi masauko aja,
Mwatuŵa m’maso mwanu
Mumayerera kale.

Ambuye Mwini moyo,
Kokoma mnafumako;
Ndizizwa pomva mawu
Umo mwachitiramo.
Chisoni chija chanu
Ncha pamachimo anga,
Mwasaukira Inu
Kupalamula kwanga.

Nditani! Bwezi langa
Kulemekeza Inu
Chifukwa cha chifundo
Ndi imfa ija yanu?
Mundikhalitse wanu,
Wokhulupira inu;
Musandilole konse
Kufulatira Inu.

Pakufa ine Mbuye
Mukhaletu pafupi,
Mundithandize ine,
E, mudzandimasula;
Ndipenyetsetsa Yesu,
Ambuye Mfumu yanga,
Ndikafa ndine wanu,
Ndikhale nanu m’Mwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version