Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

 

PANTHAWI yakufa Ambuye,
Anthu ananena:
“Dzipulumutsetu pamtandapo.”

(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O) Anafuula;
(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O)Anafuula;
“Eloyi, Eloyi
Mulungu wanga,
Mwandisiiranji,
Mwandisiiranji?”

Imfa ya Bwenzi lathu Yesu,
Yomvetsa chisoni;
Ophunzira onse anathaŵa.

Pamene anakhomedwatu,
Pamtanda Yesuyo;
Zoipa zathu zinam’psinja ‘Ye.

Imfa yake ndi yopambana,
Yotipulumutsa;
Yotitengera ife mtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 50 PAUSIKU uja,
Next: Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version