Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

 

PANTHAWI yakufa Ambuye,
Anthu ananena:
“Dzipulumutsetu pamtandapo.”

(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O) Anafuula;
(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O)Anafuula;
“Eloyi, Eloyi
Mulungu wanga,
Mwandisiiranji,
Mwandisiiranji?”

Imfa ya Bwenzi lathu Yesu,
Yomvetsa chisoni;
Ophunzira onse anathaŵa.

Pamene anakhomedwatu,
Pamtanda Yesuyo;
Zoipa zathu zinam’psinja ‘Ye.

Imfa yake ndi yopambana,
Yotipulumutsa;
Yotitengera ife mtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version