Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

 

TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
Yakuyamika Mbuye wathuyo;
Mtendere wake tiufunadi,
Titapemphera tinke kwathuko.

Titanka kwathu mkhale nafeko,
Tikufunani Yesu Mbuyathu;
Musunge ife nthaŵi zonsezo,
Mutiyeretse m’mtima mwathu mbuu!

Usiku uno mutisungedi,
Khalani m’fupi m’nyumba mwathumo;
Mamaŵanso mudzatidzutse nji!
Kuti tigwire ntchito zathuzo.

Mtitsogolere nthaŵi zonsezo;
Kuyenda tokha sitikhoza ’yi,
Ngati mukhala Mbuye m’fupimo,
Sitidzaopa kanthu kena ’yi.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version