Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

 

TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
Yakuyamika Mbuye wathuyo;
Mtendere wake tiufunadi,
Titapemphera tinke kwathuko.

Titanka kwathu mkhale nafeko,
Tikufunani Yesu Mbuyathu;
Musunge ife nthaŵi zonsezo,
Mutiyeretse m’mtima mwathu mbuu!

Usiku uno mutisungedi,
Khalani m’fupi m’nyumba mwathumo;
Mamaŵanso mudzatidzutse nji!
Kuti tigwire ntchito zathuzo.

Mtitsogolere nthaŵi zonsezo;
Kuyenda tokha sitikhoza ’yi,
Ngati mukhala Mbuye m’fupimo,
Sitidzaopa kanthu kena ’yi.

Post navigation

Previous: Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
Next: Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version