Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

  1. Home   »  
  2. Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

 

ONA Mwanawankhosayo
Wakuseza zakuipa zathu zonse.

Mwana wankhosa
Watisenzera
Zakuipa zathu zonse.

Anazenza m’thupi mwake;
Pakukhomedwa pa mtanda anali duu.

Ona pamtanda Yesuyo
Anabvutika chifukwa cha anthu’fe.

Imva kulira kwa Yesu
Pamene anasiyidwa muimfayo.

M’mwazi wake tisambamo;
Zichotsedwa zakuipa zathu zonse.

(Ona Mwana wa nkhosayo
Wakusenza zakuipa, zathu zonse.)

Post navigation

Previous: Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
Next: Hymn 50 PAUSIKU uja,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1579 Akhala mafumu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version