Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

  1. Home   »  
  2. Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

 

ONA Mwanawankhosayo
Wakuseza zakuipa zathu zonse.

Mwana wankhosa
Watisenzera
Zakuipa zathu zonse.

Anazenza m’thupi mwake;
Pakukhomedwa pa mtanda anali duu.

Ona pamtanda Yesuyo
Anabvutika chifukwa cha anthu’fe.

Imva kulira kwa Yesu
Pamene anasiyidwa muimfayo.

M’mwazi wake tisambamo;
Zichotsedwa zakuipa zathu zonse.

(Ona Mwana wa nkhosayo
Wakusenza zakuipa, zathu zonse.)

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version