Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

  1. Home   »  
  2. Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

 

NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo
Ya Mbuye, Mfumu yathu
Pofika pansipa;
Zochimwa zindizinga,
Koma ndidziŵatu
Anawombola ine
Pakundikondadi.

Ndikondwa kuti Yesu ’Nakhala mwanatu,
Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
Ndikati ndimtsatire
Zochita zakezo,
Sadzandinyoza konse
Pakundikondadi.

Pakumyamika Iye
Ndidzamwimbiratu;
Ngakhale sindimwona
Amandimveradi;
Pakuti walonjeza
Adzalandira ’ne
Ndiimbe ndi angelo,
Pakundikondadi.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version