Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

  1. Home   »  
  2. Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

 

NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo
Ya Mbuye, Mfumu yathu
Pofika pansipa;
Zochimwa zindizinga,
Koma ndidziŵatu
Anawombola ine
Pakundikondadi.

Ndikondwa kuti Yesu ’Nakhala mwanatu,
Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
Ndikati ndimtsatire
Zochita zakezo,
Sadzandinyoza konse
Pakundikondadi.

Pakumyamika Iye
Ndidzamwimbiratu;
Ngakhale sindimwona
Amandimveradi;
Pakuti walonjeza
Adzalandira ’ne
Ndiimbe ndi angelo,
Pakundikondadi.

Post navigation

Previous: Hymn 468 NDIKONDWA kuti
Next: Hymn 470 YESU andikonda ine,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version