Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

  1. Home   »  
  2. Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

 

NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo
Ya Mbuye, Mfumu yathu
Pofika pansipa;
Zochimwa zindizinga,
Koma ndidziŵatu
Anawombola ine
Pakundikondadi.

Ndikondwa kuti Yesu ’Nakhala mwanatu,
Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
Ndikati ndimtsatire
Zochita zakezo,
Sadzandinyoza konse
Pakundikondadi.

Pakumyamika Iye
Ndidzamwimbiratu;
Ngakhale sindimwona
Amandimveradi;
Pakuti walonjeza
Adzalandira ’ne
Ndiimbe ndi angelo,
Pakundikondadi.

Post navigation

Previous: Hymn 468 NDIKONDWA kuti
Next: Hymn 470 YESU andikonda ine,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version