Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

  1. Home   »  
  2. Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

 

NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo
Ya Mbuye, Mfumu yathu
Pofika pansipa;
Zochimwa zindizinga,
Koma ndidziŵatu
Anawombola ine
Pakundikondadi.

Ndikondwa kuti Yesu ’Nakhala mwanatu,
Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
Ndikati ndimtsatire
Zochita zakezo,
Sadzandinyoza konse
Pakundikondadi.

Pakumyamika Iye
Ndidzamwimbiratu;
Ngakhale sindimwona
Amandimveradi;
Pakuti walonjeza
Adzalandira ’ne
Ndiimbe ndi angelo,
Pakundikondadi.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version